Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Samueli 3:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Nthawiyi nʼkuti Samueli asanadziwe Yehova ndipo Mawu a Yehova nʼkuti asanawululidwe kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

7 Koma Samuele sanadziwe Yehova, ndiponso mau a Yehova sanaululidwe kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Koma Samuele sanadziwe Yehova, ndiponso mau a Yehova sanaululidwe kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Pamenepo nkuti Samuele asanadziŵe Chauta, ndipo mau a Chauta nkuti asanaululidwe kwa iyeyo.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 3:7
5 Mawu Ofanana  

koma ngati munthu akufuna kunyadira, anyadire chinthu ichi: kuti iye amamvetsa za Ine ndipo amandidziwa, kuti ndine Yehova, amene ndimakonda chifundo, chilungamo ndiponso ungwiro pa dziko lapansi. Zimenezi ndizo ndimakondwera nazo,” akutero Yehova.


Iye anawafunsa kuti, “Kodi munalandira Mzimu Woyera pamene munakhulupirira?” Iwo anayankha kuti, “Ayi, ife sitinamvepo kuti kuli Mzimu Woyera.”


Pamene ndinali mwana ndinkayankhula ngati mwana, ndinkaganiza ngati mwana, ndinkalingalira ngati mwana. Koma nditakula, zonse zachibwana ndinazisiya.


Yehova anayitananso, “Samueli!” Ndipo Samueli anadzuka ndi kupita kwa Eli nati, “Ndabwera popeza ndamva mukundiyitana.” Eli nati, “Mwana wanga, ine sindinakuyitane, bwerera kagone.”


Yehova anayitananso Samueli kachitatu ndipo Samueli anadzuka ndikupita kwa Eli ndipo anati, “Ndabwera popeza mwandiyitana ndithu.” Apo Eli anazindikira kuti Yehova ndiye ankayitana mnyamatayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa