1 Samueli 3:12 - Buku Lopatulika12 Tsiku lija ndidzamchitira Eli zonse ndinaneneratu za pa banja lake, kuchiyamba ndi kuchitsiriza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Tsiku lija ndidzamchitira Eli zonse ndinaneneratu za pa banja lake, kuchiyamba ndi kuchitsiriza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsiku limenelo ndidzachitadi zonse zimene ndidalankhula za Eli ndi banja lake, kuyambira pa chiyambi mpaka potsiriza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsiku limenelo ndidzachitadi zonse zimene ndinayankhula zokhudza banja la Eli kuyambira poyamba mpaka pomaliza. Onani mutuwo |