Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 28:22 - Buku Lopatulika

22 Chifukwa chake tsono, mumverenso mau a mdzakazi wanu, nimundilole kuika kakudya pamaso panu; ndipo mudye, kuti mukhale ndi mphamvu pakumuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Chifukwa chake tsono, mumverenso mau a mdzakazi wanu, nimundilole kuika kakudya pamaso panu; ndipo mudye, kuti mukhale ndi mphamvu pakumuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Nchifukwa chake tsono, inunso mumvere mau anga. Mundilole ndikuikireni kabuledi pang'ono, mudye kuti muwone nyonga zoyendera.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Tsono inunso mumvere mawu a mdzakazi wanune. Mundilole kuti ndikupatseni ka buledi pangʼono kuti mukhale ndi mphamvu zoyendera pa ulendo wanu.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 28:22
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mkaziyo anafika kwa Saulo, naona kuti ali wovutika kwambiri, nanena naye, Onani, mdzakazi wanu anamvera mau anu, ndipo ndinataya moyo wanga, ndi kumvera mau anu munalankhula ndi ine.


Koma iye anakana, nati, Sindifuna kudya. Koma anyamata ake, pamodzi ndi mkaziyo anamkakamiza; iye anamvera mau ao. Chomwecho anauka pansi, nakhala pakama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa