Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 26:22 - Buku Lopatulika

22 Davide nayankha, nati, Tapenyani mkondo wa mfumu! Abwere mnyamata wina kuutenga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Davide nayankha, nati, Tapenyani mkondo wa mfumu! Abwere mnyamata wina kuutenga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Apo Davide adayankha kuti, “Suwu mkondo wanu, mfumu. Tumani mmodzi mwa ankhondowo adzatenge.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Davide anayankha kuti, “Nawu mkondo wanu, mfumu. Tumani mmodzi wa anyamata anu abwere adzatenge.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 26:22
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo Saulo anati, Ndinachimwa; bwera, mwana wanga Davide; pakuti sindidzakuchitiranso choipa, popeza moyo wanga unali wa mtengo wapatali pamaso pako lero; ona, ndinapusa ndi kulakwa kwakukulu.


Ndipo Yehova adzabwezera munthu yense chilungamo chake ndi chikhulupiriko chake, popeza Yehova anakuperekani lero m'dzanja langa, koma sindinalole kutukulira dzanja langa pa wodzozedwa wa Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa