1 Samueli 26:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Davide anaolokera kutsidya, naima patali pamwamba paphiri; pakati pao panali danga lalikulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Davide anaolokera pa phiri; pakati pao panali danga lalikulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pambuyo pake Davide adakwerera mbali ina nakaimirira pamwamba pa phiri, pakati nkusiya mpata waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pambuyo pake Davide anadutsa nakakwerera mbali ina ya phiri, ndi kuyimirira pamwamba pa phiri patali. Pakati pawo panali mpata waukulu. Onani mutuwo |