1 Samueli 24:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo tsono taona ndidziwa kuti udzakhala mfumu ndithu, ndi kuti ufumu wa Israele udzakhazikika m'dzanja lako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo tsono taona ndidziwa kuti udzakhala mfumu ndithu, ndi kuti ufumu wa Israele udzakhazikika m'dzanja lako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ona tsono, ndikudziŵa kuti udzakhala mfumu ndithu, ndipo kuti ufumu wa Israele udzakhazikika pa iwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ona tsono, Ine ndikudziwa kuti udzakhala mfumu ndithu ndipo ufumu wa Israeli udzakhazikika mʼmanja mwako. Onani mutuwo |