1 Samueli 24:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo unatsimikiza lero lino kuti wandichitira zabwino; chifukwa sunandiphe pamene Yehova anandipereka m'dzanja lako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo unatsimikiza lero lino kuti wandichitira zabwino; chifukwa sunandipha pamene Yehova anandipereka m'dzanja lako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Lero waonetsa ubwino wako pakuti sudandiphe, Chauta atandipereka kwa iwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iweyo lero lino wandifotokozera zabwino zimene wandichitira. Yehova anandipereka mʼdzanja lako koma iwe sunandiphe. Onani mutuwo |