1 Samueli 24:14 - Buku Lopatulika14 Nanga mfumu ya Israele inatulukira yani; inu mulikupirikitsa yani? Galu wakufa, kapena nsabwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Nanga mfumu ya Israele inatulukira yani; inu mulikupirikitsa yani? Galu wakufa, kapena nsabwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kodi mfumu ya Israele yadzalondola yani? Kodi ikufuna kugwira yani? Zedi, mukulondola ine galu wakufa! Mufuna kupha ine nthata! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Kodi mfumu ya Israeli yadzalondola yani. Inu mukuthamangitsa yani? Galu wakufa kodi? Nsabwe kodi? Onani mutuwo |