Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 24:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo kunali, pakubwerera Saulo potsata Afilisti, anamuuza, kuti, Taonani, Davide ali ku chipululu cha Engedi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo kunali, pakubwerera Saulo potsata Afilisti, anamuuza, kuti, Taonani, Davide ali ku chipululu cha Engedi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Saulo atabwerako kumene ankamenyana ndi Afilisti kuja, adamva kuti Davide ali ku chipululu cha Engedi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Sauli atabwera kuchokera kumene amathamangitsa Afilisti anamva kuti, “Davide ali mʼchipululu cha Eni Gedi.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 24:1
8 Mawu Ofanana  

Chotsera woipa pamaso pa mfumu, mpando wake udzakhazikika m'chilungamo.


Mkulu akamvera chinyengo, atumiki ake onse ali oipa.


Anthu oneneza anali mwa iwe, kuti akhetse mwazi; ndipo anadya pamapiri mwa iwe, pakati pa iwe anachita zamanyazi.


Ndipo kudzachitika, kuti asodzi adzaima komweko; kuyambira pa Engedi kufikira ku Enegilaimu kudzakhala poyanikira makoka; nsomba zao zidzakhala za mitundumitundu, ngati nsomba za mu Nyanja Yaikulu, zambirimbiri.


Akondweretsa mfumu ndi zoipa zao, ndi akalonga ndi mabodza ao.


ndi Nibisani, ndi Mzinda wa Mchere, ndi Engedi; mizinda isanu ndi umodzi pamodzi ndi midzi yao.


Ndipo a ku Zifi anakwera kwa Saulo ku Gibea, nati, Davide salikubisala kwathu kodi, m'ngaka za m'nkhalango ku Horesi, m'phiri la Hakila, limene lili kumwera kwa chipululu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa