1 Samueli 23:27 - Buku Lopatulika27 Koma mthenga unafika kwa Saulo ndi kuti, Mufulumire kubwerera; popeza nkhondo yovumbulukira ya Afilisti yalowa m'dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma mthenga unafika kwa Saulo ndi kuti, Mufulumire kubwerera; popeza nkhondo yovumbulukira ya Afilisti yalowa m'dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Nthaŵi yomweyo padafika wamthenga amene adauza Saulo kuti, “Mufulumire kubwera, pakuti Afilisti akulithira nkhondo dzikoli.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Nthawi yomweyo munthu wina wamthenga anabwera kudzamuwuza Sauli kuti, “Bwerani msanga! Afilisti akuthira nkhondo dzikoli.” Onani mutuwo |