1 Samueli 22:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Saulo anati, Imva tsopano iwe mwana wa Ahitubi. Nayankha iye, Ndine, mbuye wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Saulo anati, Imva tsopano iwe mwana wa Ahitubi. Nayankha iye, Ndine, mbuye wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndipo Saulo adati, “Imva tsono, iwe mwana wa Ahitubi.” Iye adayankha kuti, “Inde, mbuyanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Sauli anati, “Tsono tamvera, mwana wa Ahitubi.” Iye anayankha kuti, “Inde mbuye wanga.” Onani mutuwo |