1 Samueli 21:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Davide anasunga mau awa mumtima mwake, naopa kwambiri Akisi mfumu ya Gati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Davide anasunga mau awa mumtima mwake, naopa kwambiri Akisi mfumu ya Gati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mau ameneŵa Davide adamloŵa mu mtima kwambiri, ndipo adayamba kuwopa Akisi mfumu ya ku Gati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mawu amenewa anamulowa kwambiri Davide mu mtima ndipo anayamba kuopa kwambiri Akisi mfumu ya ku Gati. Onani mutuwo |