1 Samueli 20:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yonatani anati, Iai ndi pang'ono ponse; ine ndikadziwa konse kuti atate wanga anatsimikiza mtima kukuchitira choipa, sindidzadziwitsa iwe kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yonatani anati, Iai ndi pang'ono ponse; ine ndikadziwa konse kuti atate wanga anatsimikiza mtima kukuchitira choipa, sindidzadziwitsa iwe kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yonatani adati, “Ai, bwanawe, nchosatheka! Ndikadadziŵa kuti abambo anga adatsimikiza zoti akuchite choipa, kodi sindikadakuuza?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yonatani anati, “Sizitheka! Ndikanadziwa kuti abambo anga atsimikiza kuti akuchite choyipa, kodi sindikanakuwuza?” Onani mutuwo |