1 Samueli 20:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo m'mawa, Yonatani ananka kuthengoko pa nthawi imene anapangana ndi Davide, ali ndi kamnyamata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo m'mawa, Yonatani ananka kuthengoko pa nthawi imene anapangana ndi Davide, ali ndi kamnyamata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 M'maŵa mwake Yonatani ndi mnyamata wake adapita kuminda kuja kumene adaapangana ndi Davide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Tsono mmawa Yonatani anapita ku munda kumene anapangana ndi Davide. Anali ndi mnyamata wake. Onani mutuwo |