1 Samueli 20:29 - Buku Lopatulika29 nati, Ndiloleni, ndimuke; chifukwa banja lathu lipereka nsembe m'mzindamo; ndi mbale wanga anandiuzitsa ndifikeko; tsono ngati wandikomera mtima undilole ndichoke, ndikaone abale anga. Chifukwa cha ichi safika ku gome la mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 nati, Ndiloleni, ndimuke; chifukwa banja lathu lipereka nsembe m'mudzimo; ndi mbale wanga anandiuzitsa ndifikeko; tsono ngati wandikomera mtima undilole ndichoke, ndikaone abale anga. Chifukwa cha ichi safika ku gome la mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Adati, ‘Undilole ndipite, popeza kuti banja lathu likupereka nsembe mumzindamo, ndipo mbale wanga adandikakamiza kuti ndikakhale nao kumeneko. Tsono ngati wandikomera mtima, undilole ndipite, kuti ndikaone abale anga.’ Nchifukwa chake sadabwere ku chakudya cha mfumu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Anati, ‘Undilole ndipite, chifukwa banja lathu likupereka nsembe mu mzindamo ndipo mʼbale wanga wandiwumiriza kuti ndikakhale nawo. Ngati wandikomera mtima, chonde ndilole ndipite ndikaone abale anga.’ Nʼchifukwa chake sanabwere kudzadya ndi mfumu.” Onani mutuwo |