1 Samueli 20:24 - Buku Lopatulika24 Chomwecho Davide anabisala kuthengo; ndipo pakukhala mwezi, mfumu inakhala pansi kudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Chomwecho Davide anabisala kuthengo; ndipo pakukhala mwezi, mfumu inakhala pansi kudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Choncho Davide adakabisala ku minda. Ndipo pamene mwezi udaoneka, mfumu Saulo adabwera ku phwando. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Choncho Davide anakabisala mʼmunda ndipo nthawi ya chikondwerero cha mwezi watsopano itakwana mfumu Sauli anadzakhala pansi kuti adye. Onani mutuwo |