Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 20:24 - Buku Lopatulika

24 Chomwecho Davide anabisala kuthengo; ndipo pakukhala mwezi, mfumu inakhala pansi kudya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Chomwecho Davide anabisala kuthengo; ndipo pakukhala mwezi, mfumu inakhala pansi kudya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Choncho Davide adakabisala ku minda. Ndipo pamene mwezi udaoneka, mfumu Saulo adabwera ku phwando.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Choncho Davide anakabisala mʼmunda ndipo nthawi ya chikondwerero cha mwezi watsopano itakwana mfumu Sauli anadzakhala pansi kuti adye.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 20:24
12 Mawu Ofanana  

Kudya masamba, pali chikondano, kuposa ng'ombe yonenepa pali udani.


Nyenyeswa youma, pokhala mtendere, iposa nyumba yodzala nyama yansembe, pali makangano.


Nsembe ya oipa inyansa; makamaka pakudza nayo iwo mwachiwembu.


Kuchita chilungamo ndi chiweruzo kupambana ndi nsembe kumkonda Yehova.


Pakuti amadya chakudya cha uchimo, namwa vinyo wa chifwamba.


Ndipo pamene mukadya si ndinu, mukamwa si ndinu kodi?


Pamenepo anamtenga Yesu kuchokera kwa Kayafa kupita ku Pretorio; koma munali mamawa; ndipo iwo sanalowe ku Pretorio, kuti angadetsedwe, koma kuti akadye Paska.


Ndipo za chija tinakambirana iwe ndi ine, taona, Yehova ali pakati pa ife nthawi zonse.


Mfumu nikhala pa mpando wake, monga ankachita nthawi zina, pa mpando wa pafupi pa khoma. Ndipo Yonatani anaimirira, ndi Abinere anakhala pa mbali ya Saulo; koma Davide anasoweka pamalo pake.


Nati Davide kwa Yonatani, Onani, mawa mwezi ukhala, ndipo ine ndiyenera kupita kukadya kwa mfumu, wosatsala; koma undilole ndikabisale kuthengo, kufikira tsiku lachitatu madzulo ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa