1 Samueli 20:22 - Buku Lopatulika22 Koma ndikati kwa mnyamatayo, Ona mivi ili kutsogoloko; pamenepo unyamuke ulendo wako; popeza Yehova wakuuza umuke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma ndikati kwa mnyamatayo, Ona mivi ili kutsogoloko; pamenepo unyamuke ulendo wako; popeza Yehova wakuuza umuke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma ndikamuuza mnyamatayo kuti, ‘Mivi ili patsogolo pako,’ pomwepo iweyo uchoke, pakuti Chauta ndiye wati uchokepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Koma ndikadzati, ‘Taona mivi ili patsogolo pako,’ iwe udzachoke chifukwa Yehova ndiye walola kuti uchokepo. Onani mutuwo |