Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 20:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo ine ndidzaponya mivi itatu pambali pake, monga ngati ndilikuponya pachandamali.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo ine ndidzaponya mivi itatu pambali pake, monga ngati ndilikuponya pachandamali.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Ine ndidzaponya mivi itatu ku mbali ina ya muluwo, ngati ndikuchita chandamale.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Ine ndidzaponya mivi itatu pambali pake, ngati ndikulasa chinthu.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 20:20
3 Mawu Ofanana  

Ndipo atapita masiku atatu, utsike msanga, nufike kumene unabisala tsiku la mlandu uja, nukhale pamwala wa Ezeri.


Ndipo taona, ndidzatumiza mnyamatayo, ndi kuti, Kafune miviyo. Ndikamuuza mwanayo, kuti, Taona mivi ili chakuno; uitole nubwere, popeza pali mtendere kwa iwe, palibe kanthu, pali Yehova.


Ndipo anauza mnyamata wakeyo, Thamanga uzikatola mivi imene ndidzaponya; ndipo analikuthamanga mnyamatayu, iye anaponya muvi kuutumphitsa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa