1 Samueli 2:24 - Buku Lopatulika24 Iai, ana anga, popeza mbiri imene ndilikuimva sili yabwino iai; mulikulakwitsa anthu a Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Iai, ana anga, popeza mbiri imene ndilikuimva sili yabwino iai; mulikulakwitsa anthu a Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Iyai ana anga, zimene ndilikumva anthu a Chauta akusimba nkumafalitsa, si zabwino ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ayi, ana anga si mbiri yabwino imene ndikumva anthu a Mulungu akufalitsa. Onani mutuwo |