1 Samueli 19:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anapita komweko ku Nayoti mu Rama; ndi mzimu wa Mulungu unamgwera iyenso; ndipo anapitirira, nanenera, mpaka anafika ku Nayoti mu Rama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anapita komweko ku Nayoti m'Rama; ndi mzimu wa Mulungu unamgwera iyenso; ndipo anapitirira, nanenera, mpaka anafika ku Nayoti m'Rama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Saulo adachoka napita ku Nayoti ku Rama. Nayenso mzimu wa Mulungu udamloŵa ndipo ankayenda akuvina namalosa mpaka kukafika ku Nayoti ku Rama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Choncho Sauli anapita ku Nayoti ku Rama. Koma Mzimu wa Mulungu unafikanso pa iye ndipo ankalosa akuyenda mpaka anafika ku Nayoti. Onani mutuwo |