Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 18:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo Saulo anamtenga tsiku lomwelo, osamlolanso apite kwao kwa atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo Saulo anamtenga tsiku lomwelo, osamlolanso apite kwao kwa atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mwakuti adamtenga Davideyo tsiku lomwelo, osamlola kuti abwerere ku banja kwa bambo wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Choncho Sauli anamusunga Davideyo kuyambira tsiku limenelo ndipo sanamulole kuti abwerere ku nyumba ya abambo ake.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 18:2
3 Mawu Ofanana  

Koma Davide akamuka kwa Saulo, nabwerera kudzadyetsa nkhosa za atate wake ku Betelehemu.


Pamenepo Yonatani anaitana Davide, namuuza zonsezi. Ndipo Yonatani anafika naye Davide kwa Saulo, iye nakhalanso pamaso pake monga kale.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa