1 Samueli 17:54 - Buku Lopatulika54 Ndipo Davide anatenga mutu wa Mfilistiyo, napita nao ku Yerusalemu; koma zida zake anazisunga m'hema wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 Ndipo Davide anatenga mutu wa Mfilistiyo, napita nao ku Yerusalemu; koma zida zake anazisunga m'hema wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Kenaka Davide adatenga mutu wa Mfilisti uja napita nawo ku Yerusalemu. Koma zida zokha za Mfilistiyo adaziika m'hema mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 Pambuyo pake Davide anatenga mutu wa Mfilisitiyo napita nawo ku Yerusalemu, koma anayika zida za Mfilisitiyo mu tenti yake. Onani mutuwo |