Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 17:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo anthuwo anamyankha motero, nati, Adzamchitira munthu wakumupha iye mwakutimwakuti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo anthuwo anamyankha motero, nati, Adzamchitira munthu wakumupha iye mwakutimwakuti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Anthu adamuuzanso zomwe zija zimene mfumu idaati idzachitire munthu wodzapha Goliyatiyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Anthu anamuwuzanso zonse zimene mfumu inanena kuti idzachitira munthu amene adzapha Mfilisitiyo.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 17:27
2 Mawu Ofanana  

Nati Aisraele, Kodi mwaona munthu uyu amene anakwera kuno? Zoonadi iye anakwera kuti adzanyoze Israele, ndipo munthu wakumupha iye, mfumu idzamlemeretsa ndi chuma chambiri, nidzampatsa mwana wake wamkazi, nidzayesa nyumba ya atate wake yaufulu mu Israele.


Napotolokera iye kwa munthu wina, nalankhula mau omwewo; ndipo anthu anamyankhanso monga momwemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa