Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 17:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo Mfilistiyo anayandikira m'mawa ndi madzulo, nadzionetsera masiku makumi anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo Mfilistiyo anayandikira m'mawa ndi madzulo, nadzionetsera masiku makumi anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Pa masiku makumi anai Goliyati uja adakhala akutuluka, namadziwonetsa m'maŵa ndi madzulo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Kwa masiku makumi anayi, Mfilisiti uja ankabwera mmawa ndi madzulo kumadzionetsera.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 17:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala.


kukayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anai. Ndipo Iye sanadye kanthu masiku awo; ndipo pamene anatha anamva njala.


Koma Davide akamuka kwa Saulo, nabwerera kudzadyetsa nkhosa za atate wake ku Betelehemu.


Ndipo Yese anati kwa Davide mwana wake, Uwatengere abale ako efa wa tirigu uyu wokazinga, ndi mikate iyi khumi, nuthamangire nazo kuzithando kwa abale ako;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa