1 Samueli 15:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo Samuele anati, Monga lupanga lako linachititsa akazi ufedwa, momwemo mai wako adzakhala mfedwa mwa akazi. Ndipo Samuele anamdula Agagi nthulinthuli pamaso pa Yehova ku Giligala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo Samuele anati, Monga lupanga lako linachititsa akazi ufedwa, momwemo mai wako adzakhala mfedwa mwa akazi. Ndipo Samuele anamdula Agagi nthulinthuli pamaso pa Yehova ku Giligala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Koma Samuele adati, “Monga momwe lupanga lako lasandutsira akazi kuti akhale opanda ana, momwemonso mai wako adzakhala wopanda mwana pakati pa akazi ena.” Ndipo Samuele adapha Agagiyo namduladula patsogolo pa guwa la Chauta ku Giligala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Koma Samueli anati, “Monga momwe lupanga lako linasandutsira amayi kukhala wopanda ana, momwemonso amayi ako adzakhala opanda mwana pakati pa amayi.” Ndipo Samueli anapha Agagi pamaso pa Yehova ku Giligala. Onani mutuwo |