Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 15:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo pakupotoloka Samuele kuti achoke, iye anagwira chilezi cha mwinjiro wake, ndipo chinang'ambika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo pakupotoloka Samuele kuti achoke, iye anagwira chilezi cha mwinjiro wake, ndipo chinang'ambika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Pamene Samuele ankatembenuka kuti azipita, Saulo adagwira mpendero wa mkanjo wake, ndipo mkanjowo udang'ambika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Samueli akutembenuka kuti azipita, Sauli anagwira mpendero wa mkanjo wake, ndipo unangʼambika.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 15:27
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ananena naye, Makhalidwe ake ndi otani? Nati iye, Nkhalamba ilikukwera yovala mwinjiro. Pamenepo Saulo anazindikira kuti ndi Samuele, naweramitsa nkhope yake pansi, namgwadira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa