Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 15:10 - Buku Lopatulika

10 Pamenepo mau a Yehova anafika kwa Samuele, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Pamenepo mau a Yehova anafika kwa Samuele, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono Chauta adauza Samuele kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kenaka Yehova anawuza Samueli kuti,

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 15:10
3 Mawu Ofanana  

Zitapita izo, mau a Yehova anadza kwa Abramu m'masomphenya, kuti, Usaope, Abramu, Ine ndine chikopa chako ndi mphotho yako yaikulukulu.


Kundichititsa chisoni kuti ndinaika Saulo akhale mfumu; pakuti wabwerera wosanditsata Ine, ndipo sanachite malamulo anga. Ndipo Samuele anakwiya; nalira kwa Yehova usiku wonse.


Koma Saulo ndi anthu anamsunga wamoyo Agagi, ndi nkhosa zokometsetsa, ndi ng'ombe, ndi zonenepa zina, ndi anaankhosa, ndi zabwino zonse sadafune kuzitha psiti; koma zonse zoipa ndi zonyansa anaziononga konsekonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa