1 Samueli 14:42 - Buku Lopatulika42 Ndipo Saulo anati, Muchite maere pakati pa ine ndi Yonatani mwana wanga. Ndipo anagwera Yonatani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Ndipo Saulo anati, Muchite maere pakati pa ine ndi Yonatani mwana wanga. Ndipo anagwera Yonatani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Tsono Saulo adati, “Chitani maere pakati pa ine ndi mwana wanga Yonatani.” Ndipo maere adagwera Yonatani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Sauli anati, “Chitani maere pakati pa ine ndi Yonatani mwana wanga.” Ndipo maere anagwera Yonatani. Onani mutuwo |