1 Samueli 14:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo ozonda a Saulo ku Gibea wa ku Benjamini anayang'ana; ndipo, onani, khamu la anthu linamwazikana, kulowa kwina ndi kwina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo ozonda a Saulo ku Gibea wa ku Benjamini anayang'ana; ndipo, onani, khamu la anthu linamwazikana, kulowa kwina ndi kwina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Alonda a Saulo a ku Gibea ku dziko la Benjamini poti ayang'ane, adangoona chigulu cha adani chikumwazikira uku ndi uku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Alonda a Sauli a ku Gibeya dziko la Benjamini atangomwaza maso anangoona chigulu cha asilikali chikumwazikana uku ndi uku. Onani mutuwo |