1 Samueli 13:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Tsono Afilisti adatuma kagulu kankhondo kukalonda mpata wa Mikimasi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Tsono gulu lina lankhondo la Chifilisti linapita kukalonda mpata wa Mikimasi. Onani mutuwo |