Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 13:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Tsono Afilisti adatuma kagulu kankhondo kukalonda mpata wa Mikimasi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Tsono gulu lina lankhondo la Chifilisti linapita kukalonda mpata wa Mikimasi.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 13:23
7 Mawu Ofanana  

Pamenepo Davide anali m'linga, ndi boma la Afilisti linali mu Betelehemu.


Wafika ku Ayati, wapitirira kunka ku Migironi; pa Mikimasi asunga akatundu ake;


wapita pampata; wagona pa Geba, Rama anthunthumira; Gibea wa Saulo wathawa.


Ndipo Afilisti anasonkhana kuti akamenyane ndi Aisraele, anali nao magaleta zikwi makumi atatu, ndi apakavalo zikwi zisanu ndi chimodzi, ndi anthu akuchuluka monga mchenga wa m'mphepete mwa nyanja. Iwowa anakwera namanga zithando ku Mikimasi kum'mawa kwa Betaveni.


Ndipo kunali tsiku lina kuti Yonatani mwana wa Saulo ananena ndi mnyamata wonyamula zida zake, Tiye tipite kunka ku kaboma ka Afilisti, tsidya lija. Koma sanauze atate wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa