1 Samueli 13:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Samuele ananena ndi Saulo, Munachita kopusa; simunasunge lamulo la Yehova Mulungu wanu, limene Iye anakulamulirani; mwenzi Yehova atakhazikitsa nthawi ino ufumu wanu, ukhale pa Israele nthawi yosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Samuele ananena ndi Saulo, Munachita kopusa; simunasunga lamulo la Yehova Mulungu wanu, limene Iye anakulamulirani; mwenzi Yehova atakhazikitsa nthawi yino ufumu wanu, ukhale pa Israele nthawi yosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Apo Samuele adamuuza kuti, “Mwachitatu zopusa. Simudatsate zimene Chauta, Mulungu wanu, adakulamulani. Mukadazitsata, bwenzi Chauta atakhazikitsa ufumu wanu pakati pa Aisraele mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Samueli anati, “Mwachita zopusa. Simunatsate zimene Yehova Mulungu wanu anakulamulani kuti muchite. Mukanazitsata, Yehova akanawukhazikitsa ufumu wanu mu Israeli mpaka kalekale. Onani mutuwo |