1 Samueli 11:4 - Buku Lopatulika4 Tsono mithengayo inafika ku Gibea kwa Saulo, nalankhula mau amenewa m'makutu a anthu; ndipo anthu onse anakweza mau, nalira misozi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tsono mithengayo inafika ku Gibea kwa Saulo, nalankhula mau amenewa m'makutu a anthu; ndipo anthu onse anakweza mau, nalira misozi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pamene amithenga adafika kwao kwa Saulo ku Gibea, nauza anthu nkhaniyo, onse adayamba kulira motaya mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Amithenga aja atafika kwawo kwa Sauli ku Gibeya ndi kufotokoza nkhaniyi kwa anthu onse, iwo analira motaya mtima. Onani mutuwo |