1 Samueli 11:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Amithenga aja atafika kwawo kwa Sauli ku Gibeya ndi kufotokoza nkhaniyi kwa anthu onse, iwo analira motaya mtima. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Tsono mithengayo inafika ku Gibea kwa Saulo, nalankhula mau amenewa m'makutu a anthu; ndipo anthu onse anakweza mau, nalira misozi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tsono mithengayo inafika ku Gibea kwa Saulo, nalankhula mau amenewa m'makutu a anthu; ndipo anthu onse anakweza mau, nalira misozi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pamene amithenga adafika kwao kwa Saulo ku Gibea, nauza anthu nkhaniyo, onse adayamba kulira motaya mtima. Onani mutuwo |