1 Samueli 10:6 - Buku Lopatulika6 ndipo Mzimu wa Yehova udzagwera inu kolimba, nanunso mudzanenera pamodzi nao, nimudzasandulika munthu wina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo Mzimu wa Yehova udzagwera inu kolimba, nanunso mudzanenera pamodzi nao, nimudzasandulika munthu wina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamenepo mzimu wa Chauta ukuloŵa mwamphamvu, ndipo nawenso uyamba kulosa nao, usinthika ndi kukhala munthu wina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kenaka Mzimu wa Yehova udzabwera pa iwe ndi mphamvu, ndipo udzayamba kulosera nawo pamodzi. Ndipo udzasinthika kukhala munthu wina. Onani mutuwo |