Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Mbiri 3:3 - Buku Lopatulika

3 wachisanu Sefatiya wa Abitala, wachisanu ndi chimodzi Itireamu wa mkazi wake Egila.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 wachisanu Sefatiya wa Abitala, wachisanu ndi chimodzi Itireamu wa mkazi wake Egila.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Mwana wake wachisanu ndi Sefatiya, mai wake anali Abitala. Mwana wake wachisanu ndi chimodzi ndi Itireamu, mai wake anali Egila.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 wachisanu anali Sefatiya, amayi ake anali Abitali; wachisanu ndi chimodzi anali Itireamu, amayi ake anali Egila.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 3:3
4 Mawu Ofanana  

ndi wachinai Adoniya mwana wa Hagiti; ndi wachisanu Sefatiya mwana wa Abitala;


ndi wachisanu ndi chimodzi Itireamu wa Egila mkazi wa Davide. Awa anambadwira Davide ku Hebroni.


wachitatu Abisalomu mwana wa Maaka mwana wamkazi wa Talimai mfumu ya Gesuri, wachinai Adoniya mwana wa Hagiti,


Anambadwira asanu ndi mmodzi mu Hebroni; ndi pomwepo anakhala mfumu zaka zisanu ndi ziwiri, ndi miyezi isanu ndi iwiri; ndi mu Yerusalemu anakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu zitatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa