Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Mbiri 3:4 - Buku Lopatulika

4 Anambadwira asanu ndi mmodzi mu Hebroni; ndi pomwepo anakhala mfumu zaka zisanu ndi ziwiri, ndi miyezi isanu ndi iwiri; ndi mu Yerusalemu anakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Anambadwira asanu ndi mmodzi m'Hebroni; ndi pomwepo anakhala mfumu zaka zisanu ndi ziwiri, ndi miyezi isanu ndi iwiri; ndi m'Yerusalemu anakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Ana asanu ndi mmodzi onseŵa adabadwira ku Hebroni, kumene adakhala mfumu pa zaka zisanu ndi ziŵiri ndi miyezi isanu ndi umodzi. Koma adakhala mfumu ku Yerusalemu zaka 33.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ana asanu ndi mmodzi awa a Davide anabadwira ku Hebroni kumene analamulirako zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi. Davide analamuliranso mu Yerusalemu kwa zaka 33,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 3:4
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anali mfumu ya nyumba ya Yuda ku Hebroni zaka zisanu ndi ziwiri kudza miyezi isanu ndi umodzi.


Ndipo masiku ake akukhala Davide mfumu ya Israele anali zaka makumi anai; zaka zisanu ndi ziwiri anakhala mfumu ku Hebroni, ndi zaka makumi atatu mphambu zitatu anakhala mfumu ku Yerusalemu.


Ndipo nthawi yoti anakhala mfumu ya Israele ndiyo zaka makumi anai; zaka zisanu ndi ziwiri anakhala mfumu mu Hebroni, ndi zaka makumi atatu anakhala mfumu mu Yerusalemu.


wachisanu Sefatiya wa Abitala, wachisanu ndi chimodzi Itireamu wa mkazi wake Egila.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa