Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Mbiri 2:2 - Buku Lopatulika

2 Dani, Yosefe, ndi Benjamini, Nafutali, Gadi, ndi Asere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Dani, Yosefe, ndi Benjamini, Nafutali, Gadi, ndi Asere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi, ndi Asere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 2:2
8 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


Ndi ana aamuna a Gadi: Zifiyoni, ndi Hagi, ndi Suni, ndi Eziboni, ndi Eri, ndi Arodi, ndi Areli.


Ndi ana aamuna a Asere: Imina, ndi Isiva, ndi Isivi, ndi Beriya, ndi Sera mlongo wao; ndi ana a Beriya: Hebere, ndi Malikiele.


Ana a Rakele mkazi wake wa Yakobo: Yosefe ndi Benjamini.


Ndi ana aamuna a Dani: Husimu.


Ndi ana aamuna a Nafutali: Yazeele, ndi Guni, ndi Yezere ndi Silemu.


Ana a Israele ndi awa: Rubeni, Simeoni, Levi, ndi Yuda, Isakara, ndi Zebuloni,


Ana a Yuda ndiwo Eri, ndi Onani, ndi Sela; Batisuwa Mkanani anambalira atatu amenewa. Koma Eri mwana woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova, ndi Iye anamupha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa