Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 2:1 - Buku Lopatulika

1 Ana a Israele ndi awa: Rubeni, Simeoni, Levi, ndi Yuda, Isakara, ndi Zebuloni,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ana a Israele ndi awa: Rubeni, Simeoni, Levi, ndi Yuda, Isakara, ndi Zebuloni,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ana a Israele naŵa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 2:1
17 Mawu Ofanana  

Ndipo anati, Dzina lako silidzatchedwanso Yakobo, koma Israele, chifukwa unayesana naye Mulungu ndithu, ndipo unapambana.


Ndipo pakutsirizika iye, pakuti anamwalira, anamutcha dzina lake Benoni; koma atate wake anamutcha Benjamini.


Sonkhanani, tamvani, ana aamuna a Yakobo; tamverani Israele atate wanu.


mfumu Magadiele, mfumu Iramu. Awa ndi mafumu a Edomu.


Dani, Yosefe, ndi Benjamini, Nafutali, Gadi, ndi Asere.


Ndipo ana a Rubeni mwana woyamba wa Israele, (pakuti ndiye mwana woyamba; koma popeza anaipsa kama wa atate wake ukulu wake unapatsidwa kwa ana a Yosefe mwana wa Israele, koma m'buku la chibadwidwe asayesedwe monga mwa ukulu wake.


ndi Yuda anabala Perezi ndi Zera mwa Tamara; ndi Perezi anabala Hezironi; ndi Hezironi anabala Ramu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa