1 Akorinto 7:6 - Buku Lopatulika6 Koma ichi ndinena monga mwa kulola, si monga mwa kulamulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma ichi ndinena monga mwa kulola, si monga mwa kulamulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamene ndikunena zimenezi, sindikuchita mokulamulani ai, koma mokulolani chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndikunena zimenezi mokulolani chabe osati mokulamulani. Onani mutuwo |