Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 6:4 - Buku Lopatulika

4 Chifukwa chake, ngati muli nayo milandu ya zinthu za moyo uno, kodi muweruzitsa iwo amene ayesedwa achabe mu Mpingo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Chifukwa chake, ngati muli nayo milandu ya zinthu za moyo uno, kodi muweruzitsa iwo amene ayesedwa achabe mu Mpingo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono ngati muli ndi milandu pa zinthu zotere, bwanji mumaika anthu amene mpingo suŵayesa kanthu kuti aiweruze?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Nʼchifukwa chake, ngati pali milandu pa zinthu zotere, sankhani anthu ena kuti akhale oweruza ngakhale alibe udindo mu mpingo.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 6:4
4 Mawu Ofanana  

Pakuti nditani nao akunja kukaweruza iwo? Kodi amene ali m'katimo simuwaweruze ndi inu,


Kodi simudziwa kuti tidzaweruza angelo? Koposa kotani nanga zinthu za moyo uno?


Ndinena ichi kukuchititsani inu manyazi. Kodi nkutero kuti mwa inu palibe mmodzi wanzeru, amene adzakhoza kuweruza pa abale,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa