1 Akorinto 5:6 - Buku Lopatulika6 Kudzitamanda kwanu sikuli bwino. Kodi simudziwa kuti chotupitsa pang'ono chitupitsa mtanda wonse? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Kudzitamanda kwanu sikuli bwino. Kodi simudziwa kuti chotupitsa pang'ono chitupitsa mtanda wonse? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamenepo palibe choti inu nkunyadira ai. Kodi simuŵadziŵa mau aja akuti, “Chofufumitsira buledi chapang'ono chimafufumitsa mkate wonse?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kudziwa kwanu si kwabwino. Kodi simukudziwa kuti yisiti wochepa amafufumitsa mphumphu yaufa wonse wa tirigu? Onani mutuwo |