1 Akorinto 5:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo mukhala odzitukumula, kosati makamaka mwachita chisoni, kuti achotsedwe pakati pa inu iye amene anachita ntchito iyi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo mukhala odzitukumula, kosati makamaka mwachita chisoni, kuti achotsedwe pakati pa inu iye amene anachita ntchito iyi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndipo inu mukudzitukumulabe! Kwenikweni mukadayenera kumva chisoni, ndi kumchotsa pakati panu munthu amene adachita zimeneziyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo inu mukudzitukumulabe. Kodi simukanayenera kudzazidwa ndi chisoni ndipo mukanamuchotsa pa chiyanjano chanu munthu wochita zimenezi? Onani mutuwo |