1 Akorinto 4:21 - Buku Lopatulika21 Kodi ndifike kwa inu ndi ndodo, kapena mwachikondi, ndi mzimu wakufatsa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Kodi ndifike kwa inu ndi ndodo, kapena mwachikondi, ndi mzimu wakufatsa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Nanga mukufuna chiyani? Mukufuna kuti ndidzabwere kwanuko ndi mkwapulo, kapena ndi mtima wachikondi ndi wofatsa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kodi musankha chiyani? Kodi ndidzabwere ndi chikwapu, kapena mu chikondi ndiponso mwa mzimu wofatsa? Onani mutuwo |