1 Akorinto 4:1 - Buku Lopatulika1 Chotero munthu atiyese ife, monga atumiki a Khristu, ndi adindo a zinsinsi za Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chotero munthu atiyese ife, monga atumiki a Khristu, ndi adindo a zinsinsi za Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Muzitiwona ngati antchito a Khristu, ngati akapitao osamala zinsinsi za Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Choncho tsono anthu atione ife monga atumiki a Khristu, ndiponso ngati osunga zinsinsi za Mulungu. Onani mutuwo |