1 Akorinto 3:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; chilimo cha Mulungu, chimango cha Mulungu ndi inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; chilimo cha Mulungu, chimango cha Mulungu ndi inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Komabe ife ndife okhaokha ogwira ntchito ya Mulungu, inuyo ndinu munda wa Mulungu, ndinunso nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; inu ndinu munda wa Mulungu, Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwo |