1 Akorinto 3:20 - Buku Lopatulika20 ndiponso Ambuye azindikira zolingirira za anzeru, kuti zili zopanda pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndiponso Ambuye azindikira zolingirira za anzeru, kuti zili zopanda pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Penanso Malembo akuti, “Ambuye amaŵadziŵa maganizo a anthu anzeru kuti ndi achabe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 ndiponso, “Ambuye amadziwa kuti maganizo a wanzeru ndi opandapake.” Onani mutuwo |