1 Akorinto 3:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti palibe munthu akhoza kuika maziko ena, koma amene aikidwako, ndiwo Yesu Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti palibe munthu akhoza kuika maziko ena, koma amene aikidwako, ndiwo Yesu Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pajatu palibe maziko enanso amene wina aliyense angathe kukhazika osiyana ndi maziko amene alipo kale. Mazikowo ndi Yesu Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pakuti wina sangayikenso maziko ena oposera amene anakhazikitsidwa kale, amene ndi Yesu Khristu. Onani mutuwo |