1 Akorinto 15:51 - Buku Lopatulika51 Taonani, ndikuuzani chinsinsi; sitidzagona tonse, koma tonse tidzasandulika, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Taonani, ndikuuzani chinsinsi; sitidzagona tonse, koma tonse tidzasandulika, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Mvetsetsani, ndikuuzeni chinsinsi. Sikuti tonse tidzamwalira, komabe tonse tidzasandulika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Tamverani, ndikuwuzeni chinsinsi. Tonse sitidzagona tulo, koma tonse tidzasandulika. Onani mutuwo |