1 Akorinto 14:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti ngati lipenga lipereka mau osazindikirika, adzadzikonzera ndani kunkhondo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti ngati lipenga lipereka mau osazindikirika, adzadzikonzera ndani kunkhondo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndiponso woliza lipenga akapanda kuliliza momveka bwino, ndani angakonzekere nkhondo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Komanso ngati lipenga silimveka bwino, ndani angakonzekere nkhondo? Onani mutuwo |