Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 14:8 - Buku Lopatulika

8 Pakuti ngati lipenga lipereka mau osazindikirika, adzadzikonzera ndani kunkhondo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Pakuti ngati lipenga lipereka mau osazindikirika, adzadzikonzera ndani kunkhondo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ndiponso woliza lipenga akapanda kuliliza momveka bwino, ndani angakonzekere nkhondo?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Komanso ngati lipenga silimveka bwino, ndani angakonzekere nkhondo?

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 14:8
12 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala tsiku limenelo, lipenga lalikulu lidzaombedwa; ndipo adzafika omwe akadatayika m'dziko la Asiriya, ndi opirikitsidwa a m'dziko la Ejipito; ndipo adzapembedza Yehova m'phiri lopatulika la pa Yerusalemu.


Matumbo anga, matumbo anga! Ndipoteka pamtima panga penipeni; mtima wanga sukhala pansi m'kati mwanga; sindithai kutonthola; pakuti wamva, moyo wanga, mau a lipenga, mbiri ya nkhondo.


Muombe lipenga mu Ziyoni, nimufuulitse m'phiri langa lopatulika; onse okhala m'dziko anjenjemere; pakuti tsiku la Yehova lilinkudza, pakuti liyandikira;


Kodi adzaomba lipenga m'mzinda osanjenjemera anthu? Kodi choipa chidzagwera mzinda osachichita Yehova?


Ndipo pamene mupita kunkhondo m'dziko lanu kuchita nkhondo pa mdani wakusautsa inu, mulize chokweza ndi malipenga; ndipo Yehova Mulungu wanu adzakumbukira inu, nadzakupulumutsani kwa adani anu.


Ngakhale zinthu zopanda moyo, zopereka mau, ngati chitoliro, kapena ngoli, ngati sizisiyanitsa maliridwe, chidzazindikirika bwanji chimene chiombedwa kapena kuimbidwa?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa