1 Akorinto 13:8 - Buku Lopatulika8 Chikondi sichitha nthawi zonse, koma kapena zonenera zidzakhala chabe, kapena malilime adzaleka, kapena nzeru idzakhala chabe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chikondi sichitha nthawi zonse, koma kapena zonenera zidzakhala chabe, kapena malilime adzaleka, kapena nzeru idzakhala chabe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chikondi nchosatha. Uneneri udzatha, kulankhula zilankhulo zosadziŵika kudzalekeka, ndipo nzeru za anthu zidzatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Chikondi ndi chosatha. Koma mphatso ya uneneri idzatha, pamene pali kuyankhula malilime adzatha, pamene pali chidziwitso chidzatha. Onani mutuwo |